1 Mbiri 3:13-17 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

13. Ahazi mwana wace, Hezekiya mwana wace, Manase mwana wace,

14. Amoni mwana wace, Yosiya mwana wace.

15. Ndi ana a Yosiya: woyamba Yohanana, waciwiri Yehoyakimu, wacitatu Zedekiya, wacinai Salumu.

16. Ndi ana a Yehoyakimu: Yekoniya mwana wace, Zedekiya mwana wace.

17. Ndi mwana wa Yekoniya: Asiri, Sealitiyeli mwana wace,

1 Mbiri 3