1 Mbiri 24:26-30 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

26. Ana a Merari: Mali ndi Musi; mwana wa Yaziya, Beno.

27. Ana a Merari: wa Yaziya, Beno, ndi Sohamu, ndi Sakuri, ndi Ibri.

28. Wa Mali: Eleazara, ndiye wopanda ana.

29. Wa Kisi: mwana wa Kisi, Yerameli.

30. Ndi ana a Musi: Mali, ndi Ederi, ndi Yerimoti, Awa ndi ana a Alevi monga mwa nyumba za makolo ao.

1 Mbiri 24