1 Mbiri 24:22-30 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

22. Wa Aizari: Selomoti; wa ana a Selomoti, Yahati.

23. Ndi wa ana a Hebroni: mkuru ndi Yeriya, waciwiri Amariya, wacitatu Yahazieli, wacinai Yekameamu.

24. Wa ana a Uziyeli, Mika; wa ana a Mika, Samiri.

25. Mbale wa Mika, Isiya; a ana a Isiya, Zekariya,

26. Ana a Merari: Mali ndi Musi; mwana wa Yaziya, Beno.

27. Ana a Merari: wa Yaziya, Beno, ndi Sohamu, ndi Sakuri, ndi Ibri.

28. Wa Mali: Eleazara, ndiye wopanda ana.

29. Wa Kisi: mwana wa Kisi, Yerameli.

30. Ndi ana a Musi: Mali, ndi Ederi, ndi Yerimoti, Awa ndi ana a Alevi monga mwa nyumba za makolo ao.

1 Mbiri 24