1 Mbiri 23:25-27 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

25. Pakuti Davide anati, Yehova Mulungu wa Israyeli wapumulitsa anthu ace; ndipo akhala m'Yerusalemu kosatha;

26. ndiponso Alevi asasenzenso kacisi ndi zipangizo zace zonse za utumiki wace.

27. Pakuti monga mwa mau ace otsiriza a Davide, ana a Levi anawerengedwa kuyambira a zaka makumi awiri ndi mphambu.

1 Mbiri 23