1 Mbiri 17:11 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo kudzacitika, atakwanira masiku ako kuti uzipita kukhala ndi makolo ako, ndidzaukitsa mbeu yako pambuyo pako, ndiye wa ana ako; ndipo ndidzakhazikitsa ufumu wace.

1 Mbiri 17

1 Mbiri 17:3-14