1 Mbiri 15:26 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo popeza Mulungu anathandiza Alevi akusenza likasa la cipangano la Yehova, iwo anapha nsembe ng'ombe zisanu ndi ziwiri, ndi nkhosa zamphongo zisanu ndi ziwiri.

1 Mbiri 15

1 Mbiri 15:19-27