1 Mbiri 15:2 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Pamenepo Davide anati, Sayenera ena kusenza likasa la Mulungu koma Alevi ndiwo; pakuti Yehova anawasankha iwo kusenza likasa la Mulungu, ndi kumtumikira iye kosatha.

1 Mbiri 15

1 Mbiri 15:1-5