1 Mafumu 9:17-20 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

17. Ndipo Solomo anamanganso Gezeri, ndi Betihoroni wakunsi,

18. ndi Balati, ndi Tadimori wa m'cipululu m'dziko muja,

19. ndi midzi yonse yosungamo zinthu zace za Solomo, ndi midzi yosungamo magareta ace, ndi midzi yokhalamo apakavalo ace, ndi zina ziti zonse zidakomera Solomo kuzimanga m'Yerusalemu, ndi ku Lebano, ndi m'dziko lonse la ufumu wace.

20. Ndipo Aamori, ndi Ahiti, ndi Aperizi, ndi Ahivi, ndi Ayebusi otsala, amene sanali a ana a Israyeli,

1 Mafumu 9