1 Atesalonika 2:9 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Pakuti mukumbukila, abale, cigwiritso cathu ndi cibvuto cathu; pocita usiku ndi usana, kuti tingalemetse wina wa inu, tinalalikira kwa inu Uthenga Wabwino wa Mulungu.

1 Atesalonika 2

1 Atesalonika 2:5-12